Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:54 - Buku Lopatulika

54 Ndipo pamenepo anamgwira Iye, napita naye, nalowa m'nyumba ya mkulu wa ansembe. Koma Petro anatsata kutali.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 Ndipo pamenepo anamgwira Iye, napita naye, nalowa m'nyumba ya mkulu wa ansembe. Koma Petro anatsata kutali.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 Anthu aja adamugwira Yesu, napita naye ku nyumba ya mkulu wa ansembe onse. Petro ankaŵatsatira chapatali.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 Pamenepo anamugwira Iye, napita naye ndipo anamutengera ku nyumba ya mkulu wa ansembe. Petro anamutsatira patali.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:54
7 Mawu Ofanana  

Koma pokhala naye akazembe a akalonga a ku Babiloni, amene anatumiza kwa iye kufunsira za chodabwitsa chija chidachitika m'dzikomo, Mulungu anamsiya, kumuyesa, kuti adziwe zonse za mumtima mwake.


Masiku onse, pamene ndinali ndi inu mu Kachisi, simunatanse manja anu kundigwira: koma nyengo ino ndi yanu, ndipo ulamuliro wa mdima ndi wanu.


Koma Anasi adamtumiza Iye womangidwa kwa Kayafa mkulu wa ansembe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa