Luka 22:53 - Buku Lopatulika53 Masiku onse, pamene ndinali ndi inu mu Kachisi, simunatanse manja anu kundigwira: koma nyengo ino ndi yanu, ndipo ulamuliro wa mdima ndi wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201453 Masiku onse, pamene ndinali ndi inu m'Kachisi, simunatansa manja anu kundigwira: koma nyengo yino ndi yanu, ndipo ulamuliro wa mdima ndi wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa53 Tsiku ndi tsiku ndidaali nanu m'Nyumba ya Mulungu, inuyo osandigwira. Koma ino ndi nthaŵi yanu ndiponso ya mphamvu za mdima.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero53 Tsiku lililonse ndinali nanu mʼmabwalo a mʼNyumba ya Mulungu ndipo inu simunandigwire. Koma iyi ndi nthawi yanu pamene mdima ukulamulira.” Onani mutuwo |