Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:47 - Buku Lopatulika

47 Pamene Iye anali chilankhulire, taonani, khamu la anthu, ndipo iye wotchedwa Yudasi, mmodzi wa khumi ndi awiriwo, anawatsogolera; nayandikira Yesu kumpsompsona Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

47 Pamene Iye anali chilankhulire, taonani, khamu la anthu, ndipo iye wotchedwa Yudasi, mmodzi wa khumi ndi awiriwo, anawatsogolera; nayandikira Yesu kumpsompsona Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

47 Yesu akulankhula choncho, padabwera khamu la anthu. Amene ankaŵatsogolera anali Yudasi, mmodzi mwa ophunzira khumi ndi aŵiri aja. Iyeyu adadza pafupi ndi Yesu kuti amumpsompsone.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

47 Pamene Iye ankayankhulabe, gulu la anthu linabwera, ndipo munthu wotchedwa Yudasi, mmodzi wa khumi ndi awiriwo analitsogolera. Iye anamuyandikira Yesu kuti amupsompsone.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:47
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Yudasi Iskariote, ndiye mmodzi wa khumi ndi awiriwo, anachoka napita kwa ansembe aakulu, kuti akampereke Iye kwa iwo.


Koma Yesu anati kwa iye, Yudasi, ulikupereka Mwana wa Munthu ndi chimpsompsono kodi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa