Luka 22:48 - Buku Lopatulika48 Koma Yesu anati kwa iye, Yudasi, ulikupereka Mwana wa Munthu ndi chimpsompsono kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Koma Yesu anati kwa iye, Yudasi, ulikupereka Mwana wa Munthu ndi chimpsompsono kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Koma Yesu adamufunsa kuti, “Yudasi, mongadi ukupereka Mwana wa Munthu kwa adani pakumumpsompsona?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Koma Yesu anamufunsa kuti, “Yudasi, kodi ukupereka Mwana wa Munthu ndi mpsopsono?” Onani mutuwo |