Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 22:46 - Buku Lopatulika

46 ndipo anati kwa iwo, Mugoneranji? Ukani, pempherani kuti mungalowe m'kuyesedwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

46 ndipo anati kwa iwo, Mugoneranji? Ukani, pempherani kuti mungalowe m'kuyesedwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

46 ndipo adaŵafunsa kuti, “Bwanji mukugona? Dzukani ndi kumapemphera, kuti mungagwe m'zokuyesani.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

46 Iye anafunsa kuti, Nʼchifukwa chiyani mukugona? “Dzukani ndipo pempherani kuti inu musagwe mʼmayesero.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:46
5 Mawu Ofanana  

Ndipo mwini chombo anadza kwa iye, nanena naye, Utani iwe wam'tulo? Uka, itana Mulungu wako, kapena Mulunguyo adzatikumbukira tingatayike.


Ndipo pofika pomwepo, anati kwa iwo, Pempherani kuti mungalowe m'kuyesedwa.


Ndipo pamene ananyamuka pakupemphera anadza kwa ophunzira, nawapeza ali m'tulo ndi chisoni,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa