Luka 22:42 - Buku Lopatulika42 nati, Atate, mukafuna Inu, chotsani chikho ichi pa Ine; koma si kufuna kwanga ai, komatu kwanu kuchitike. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 nati, Atate, mukafuna Inu, chotsani chikho ichi pa Ine; koma si kufuna kwanga ai, komatu kwanu kuchitike. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Adati, “Atate, ngati mukufuna, mundichotsere chikho chamasautsochi. Komabe muchite zimene mukufuna Inu, osati zimene ndikufuna Ine ai.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 “Atate ngati mukufuna chotsereni chikho ichi. Komatu muchite zimene mukufuna osati zimene ndikufuna ine.” Onani mutuwo |