Luka 22:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo anapatukana nao kutalika kwake ngati kuponya mwala, nagwada pansi napemphera, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo anapatukana nao kutalika kwake ngati kuponya mwala, nagwada pansi napemphera, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Tsono adapatukana nawo kadera, kutalika kwake ngati pamene mwala ungafike munthu atauponya. Apo adagwada pansi nayamba kupemphera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Iye anapita patsogolo pangʼono patali ngati kuponya mwala, anagwada napephera kuti, Onani mutuwo |