Luka 22:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo pofika pomwepo, anati kwa iwo, Pempherani kuti mungalowe m'kuyesedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo pofika pomwepo, anati kwa iwo, Pempherani kuti mungalowe m'kuyesedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Pamene adafika kumeneko, Yesu adaŵauza kuti, “Pempherani, kuti mungagwe m'zokuyesani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Atafika pamalopo, Iye anawawuza kuti, “Pempherani kuti musagwe mʼmayesero.” Onani mutuwo |