Luka 22:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo Iye anatuluka, napita monga ankachitira, kuphiri la Azitona; ndi ophunzira anamtsata Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo Iye anatuluka, napita monga ankachitira, kuphiri la Azitona; ndi ophunzira anamtsata Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Pambuyo pake Yesu adatuluka mu mzinda napita ku Phiri la Olivi monga adaazoloŵera. Ndipo ophunzira ake adapita naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Yesu anapitanso monga mwa masiku onse ku Phiri la Olivi, ndipo ophunzira ake anamutsatira Iye. Onani mutuwo |