Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 22:38 - Buku Lopatulika

38 Ndipo iwo anati, Ambuye, taonani, malupanga awiri siwa. Ndipo anati kwa iwo, Chakwanira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ndipo iwo anati, Ambuye, taonani, malupanga awiri siwa. Ndipo anati kwa iwo, Chakwanira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Ophunzirawo adati, “Ambuye, aŵa malupanga, tili nawo kale aŵiri.” Yesu adaŵauza kuti, “Chabwino, basi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Ophunzira anati, “Taonani Ambuye, awa malupanga awiri.” Iye anayankha kuti, “Amenewa akwanira.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:38
9 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, mmodzi wa iwo anali pamodzi ndi Yesu, anatansa dzanja lake, nasolola lupanga lake, nakantha kapolo wa mkulu wa ansembe, nadula khutu lake.


Ndipo anati kwa iwo, Koma tsopano, iye amene ali ndi thumba la ndalama, alitenge, ndi thumba la kamba lomwe; ndipo amene alibe, agulitse chofunda chake, nagule lupanga.


Ndipo m'mene iwo akumzinga Iye anaona chimene chiti chichitike, anati, Ambuye, tidzakantha ndi lupanga kodi?


Yesu anayankha, Ufumu wanga suli wa dziko lino lapansi; ufumu wanga ukadakhala wa dziko lino lapansi, anyamata anga akadalimbika nkhondo, kuti ndisaperekedwe kwa Ayuda; koma tsopano ufumu wanga suli wochokera konkuno.


Koma ife popeza tili a usana tisaledzere, titavala chapachifuwa cha chikhulupiriro ndi chikondi; ndi chisoti chili chiyembekezo cha chipulumutso.


ameneyo mumkanize okhazikika m'chikhulupiriro, podziwa kuti zowawa zomwezo zilimkukwaniridwa pa abale anu ali m'dziko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa