Luka 22:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo iwo anati, Ambuye, taonani, malupanga awiri siwa. Ndipo anati kwa iwo, Chakwanira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo iwo anati, Ambuye, taonani, malupanga awiri siwa. Ndipo anati kwa iwo, Chakwanira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Ophunzirawo adati, “Ambuye, aŵa malupanga, tili nawo kale aŵiri.” Yesu adaŵauza kuti, “Chabwino, basi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Ophunzira anati, “Taonani Ambuye, awa malupanga awiri.” Iye anayankha kuti, “Amenewa akwanira.” Onani mutuwo |