Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:43 - Buku Lopatulika

43 Ndipo anamuonekera Iye mngelo wa Kumwamba namlimbitsa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 Ndipo anamuonekera Iye mngelo wa Kumwamba namlimbitsa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 [Pamenepo mngelo wochokera Kumwamba adamuwonekera namlimbitsa mtima.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 Mngelo wochokera kumwamba anafika namulimbikitsa.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:43
16 Mawu Ofanana  

Ndipo ine, chaka choyamba cha Dariusi Mmedi, ndinauka kumlimbikitsa ndi kumkhazikitsa.


Kapena uganiza kuti sindingathe kupemphera Atate wanga, ndipo Iye adzanditumizira tsopano lino mabungwe a angelo oposa khumi ndi awiri?


Pomwepo mdierekezi anamsiya Iye, ndipo onani, angelo anadza, namtumikira Iye.


nanena naye, Ngati muli Mwana wa Mulungu, mudzigwetse nokha pansi: pakuti kwalembedwa, kuti, Adzalamula angelo ake za iwe, ndipo pa manja ao adzakunyamula iwe, ungagunde konse phazi lako pamwala.


koma ndinakupempherera kuti chikhulupiriro chako chingazime; ndipo iwe, pamene watembenuka ukhazikitse abale ako.


nalimbikitsa mitima ya ophunzira, nadandaulira iwo kuti akhalebe m'chikhulupiriro, ndi kuti tiyenera kulowa mu ufumu wa Mulungu ndi zisautso zambiri.


Atakhala kumeneko nthawi, anachoka, napita ku madera osiyanasiyana a dziko la Galatiya ndi la Frijiya, nakhazikitsa ophunzira onse.


Koma langiza Yoswa, numlimbitse mtima, ndi kumkhwimitsa, pakuti adzaoloka pamaso pa anthu awa, nadzawalandiritsa dziko ulionali likhale laolao.


Ndipo povomerezeka, chinsinsi cha kuchitira Mulungu ulemu nchachikulu: Iye amene anaonekera m'thupi, anayesedwa wolungama mumzimu, anapenyeka ndi angelo, analalikidwa mwa amitundu, wokhulupiridwa m'dziko lapansi, wolandiridwa mu ulemerero.


Kodi siili yonse mizimu yotumikira, yotumidwa kuti itumikire iwo amene adzalowa chipulumutso?


Ndipo pamene atenganso wobadwa woyamba kulowa naye m'dziko, anena, Ndipo amgwadire Iye angelo onse a Mulungu.


Potero kudamuyenera kufanizidwa ndi abale m'zonse, kuti akadzakhala mkulu wa ansembe wachifundo ndi wokhulupirika m'zinthu za kwa Mulungu, kuti apereke dipo la zoipa za anthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa