Luka 22:32 - Buku Lopatulika32 koma ndinakupempherera kuti chikhulupiriro chako chingazime; ndipo iwe, pamene watembenuka ukhazikitse abale ako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 koma ndinakupempherera kuti chikhulupiriro chako chingazime; ndipo iwe, pamene watembenuka ukhazikitse abale ako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Koma Ine ndakupempherera, kuti usaleke kundikhulupirira. Ndipo iweyo utatembenuka mtima, ukaŵalimbitse abale akoŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Koma Ine ndakupempherera Simoni, kuti chikhulupiriro chako chisafowoke ndipo pamene udzabwerera kwa Ine, udzalimbikitse abale ako.” Onani mutuwo |