Luka 22:31 - Buku Lopatulika31 Simoni, Simoni, taona, Satana anafunsa akutengeni kuti akupeteni ngati tirigu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Simoni, Simoni, taona, Satana anafunsa akutengeni kuti akupeteni ngati tirigu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 “Simoni, Simoni, chenjera! Mulungu walola Satana kuti akupeteni nonse ngati tirigu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 “Simoni, Simoni, Satana wapempha kuti akupete ngati tirigu. Onani mutuwo |