Luka 22:30 - Buku Lopatulika30 ndipo mudzakhala pa mipando yachifumu ndi kuweruza mafuko khumi ndi awiri a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 ndipo mudzakhala pa mipando yachifumu ndi kuweruza mafuko khumi ndi awiri a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Ndikadzaloŵa mu ufumu wanga, muzidzadya ndi kumwa pamodzi nane, ndipo mudzakhala pa mipando yachifumu nkumaweruza mafuko khumi ndi aŵiri a Israele.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 kuti inu muthe kudya ndi kumwa pa tebulo langa mu ufumu wanga ndi kukhala pa mipando yaufumu kuweruza mafuko khumi ndi awiri a Israeli.” Onani mutuwo |