Luka 22:29 - Buku Lopatulika29 ndipo Ine ndikuikirani ufumu, monganso Atate wanga anandiikira Ine, kuti mukadye ndi kumwa kugome kwanga mu Ufumu wanga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 ndipo Ine ndikuikirani ufumu, monganso Atate wanga anandiikira Ine, kuti mukadye ndi kumwa kugome kwanga mu Ufumu wanga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Nchifukwa chake, monga Atate anga adandipatsa ufumu, Inenso ndikukupatsani ufumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Ndipo Ine ndikupatsani inu ufumu, monga momwe Atate anga anandipatsiranso Ine, Onani mutuwo |