Luka 22:33 - Buku Lopatulika33 Ndipo anati kwa Iye, Ambuye, ndilipo ndikapite ndi Inu kundende ndi kuimfa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Ndipo anati kwa Iye, Ambuye, ndilipo ndikapite ndi Inu kundende ndi kuimfa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Apo Petro adati, “Ambuye, ndili wokonzeka kupita nanu ku ndende, ngakhale kufa kumene.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Koma iye anayankha kuti, “Ambuye, ndine wokonzeka kupita nanu ku ndende ndi kufa komwe.” Onani mutuwo |