Luka 22:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Satana analowa mwa Yudasi wonenedwa Iskariote, amene anawerengedwa mmodzi wa khumi ndi awiriwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Satana analowa mwa Yudasi wonenedwa Iskariote, amene anawerengedwa mmodzi wa khumi ndi awiriwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono Satana adamuloŵa Yudasi wotchedwa Iskariote, amene anali mmodzi mwa ophunzira khumi ndi aŵiri aja a Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kenaka Satana analowa mwa Yudasi, wotchedwa Isikarioti, mmodzi wa khumi ndi a iwiriwo. Onani mutuwo |