Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo anati kwa iwo, Mafumu a anthu a mitundu awachitira ufumu; ndipo iwo amene awachitira ulamuliro anenedwa, Ochitira zabwino.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo anati kwa iwo, Mafumu a anthu a mitundu awachitira ufumu; ndipo iwo amene awachitira ulamuliro anenedwa, Ochitira zabwino.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Yesu adaŵauza kuti, “Pakati pa anthu akunja, mafumu amadyera anthu ao masuku pa mutu, ndipo amene amaŵaonetsa mphamvu zao, amatchedwa mfulu zopatsa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Yesu anawawuza kuti, “Mafumu a anthu a mitundu ina amaonetsa mphamvu za ufumu wawo pa anthuwo; ndipo amene ali ndi ulamuliro, amapatsidwa dzina la kuti ‘Opindula.’

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:25
2 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa