Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo kunakhala kutsutsana mwa iwo, ndani wa iwo ayesedwe wamkulu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo kunakhala kutsutsana mwa iwo, ndani wa iwo ayesedwe wamkulu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Tsono ophunzira aja adayamba kutsutsana kuti, “Kodi mwa ife amati wamkulu ndani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Komanso mkangano unabuka pakati pawo kuti ndani mwa iwo amene amaganiziridwa kukhala wamkulu.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:24
11 Mawu Ofanana  

Nthawi yomweyo ophunzira anadza kwa Yesu, nanena, Ndani kodi ali wopambana mu Ufumu wa Kumwamba?


Koma iwo anakhala chete; pakuti anatsutsana wina ndi mnzake panjira, kuti, wamkulu ndani?


Ndipo anayamba kufunsana mwa iwo okha, ndiye yani mwa iwo amene adzachita ichi.


Ndipo anayamba kutsutsana kuti wamkulu mwa iwo ndani.


M'chikondano cha anzanu wina ndi mnzake mukondane ndi chikondi chenicheni; mutsogolerane ndi kuchitira wina mnzake ulemu;


Chikondi chikhala chilezere, chili chokoma mtima; chikondi sichidukidwa; chikondi sichidziwa kudzitamanda, sichidzikuza,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa