Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo anayamba kufunsana mwa iwo okha, ndiye yani mwa iwo amene adzachita ichi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo anayamba kufunsana mwa iwo okha, ndiye yani mwa iwo amene adzachita ichi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Apo onse adayamba kumafunsana kuti, “Kodi ndani mwa ife angachite zotere?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Iwo anayamba kufunsana pakati pawo kuti ndi ndani wa iwo amene akanachita ichi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:23
5 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anagwidwa ndi chisoni chachikulu, nayamba kunena kwa Iye mmodzimmodzi, Kodi ndine, Ambuye?


Anayamba iwo kukhala ndi chisoni, ndi kunena naye mmodzimmodzi, kuti, Ndine kodi?


Pakuti Mwana wa Munthu amukatu, monga kunaikidwiratu; koma tsoka munthuyo amene ampereka!


Ndipo kunakhala kutsutsana mwa iwo, ndani wa iwo ayesedwe wamkulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa