Luka 22:22 - Buku Lopatulika22 Pakuti Mwana wa Munthu amukatu, monga kunaikidwiratu; koma tsoka munthuyo amene ampereka! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pakuti Mwana wa Munthu amukatu, monga kunaikidwiratu; koma tsoka munthuyo amene ampereka! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Mwana wa Munthu akukaphedwadi, monga momwe Mulungu adazikonzeratu kale. Komabe ali ndi tsoka munthu amene akukapereka Mwana wa Munthuyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Mwana wa Munthu apita monga mmene zinalembedwera, koma tsoka kwa munthu amene amupereka Iye.” Onani mutuwo |