Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:21 - Buku Lopatulika

21 Koma onani, dzanja lake la iye amene adzandipereka ali pagome pano pamodzi ndi Ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Koma onani, dzanja lake la iye amene adzandipereka ali pagome pano pamodzi ndi Ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 “Koma ndithudi wondipereka kwa adani akudya nane pamodzi pompano.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Koma dzanja la amene akundipereka Ine lili pamodzi ndi langa pa chakudya pano.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:21
9 Mawu Ofanana  

mabwenzi anga enieni onse anyansidwa nane; ndi onse ndakondana nao asandulika adani anga.


Ngakhale bwenzi langa lenileni, amene ndamkhulupirira, ndiye amene adadyako mkate wanga, anandikwezera chidendene chake.


Ndipo pofika madzulo anadza Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.


Ndipo Yesu anayankha, Ndi iyeyu, amene Ine ndidzamsunsira nthongo ndi kumpatsa. Pamenepo, m'mene anasunsa nthongo anaitenga naipatsa Yudasi mwana wa Simoni Iskariote.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa