Luka 22:21 - Buku Lopatulika21 Koma onani, dzanja lake la iye amene adzandipereka ali pagome pano pamodzi ndi Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Koma onani, dzanja lake la iye amene adzandipereka ali pagome pano pamodzi ndi Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 “Koma ndithudi wondipereka kwa adani akudya nane pamodzi pompano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Koma dzanja la amene akundipereka Ine lili pamodzi ndi langa pa chakudya pano. Onani mutuwo |