Luka 22:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo analandira chikho, ndipo pamene adayamika, anati, Landirani ichi, muchigawane mwa inu nokha; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo analandira chikho, ndipo pamene adayamika, anati, Landirani ichi, muchigawane mwa inu nokha; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Atatero Yesu adatenga chikho, ndipo atathokoza Mulungu, adati, “Kwayani, imwani nonsenu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Atanyamula chikho, Iye anayamika ndipo anati, “Tengani ndipo patsiranani pakati panu. Onani mutuwo |