Luka 22:18 - Buku Lopatulika18 pakuti ndinena kwa inu, kuyambira tsopano Ine sindidzamwako chipatso cha mpesa, kufikira Ufumu wa Mulungu udzafika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 pakuti ndinena kwa inu, kuyambira tsopano Ine sindidzamwako chipatso cha mpesa, kufikira Ufumu wa Mulungu udzafika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndithu ndikunenetsa kuti kuyambira tsopano sindidzamwanso konse chakumwa cha mtengo wamphesa, mpaka Mulungu atadzakhazikitsa ufumu wake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pakuti ndikukuwuzani kuti, Ine sindidzamwanso zochokera ku chipatso cha mphesa mpaka ufumu wa Mulungu utabwera.” Onani mutuwo |