Luka 22:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo anati kwa iwo, Ndinalakalaka ndithu kudya Paska uwu pamodzi ndinu, ndisanayambe kusautsidwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo anati kwa iwo, Ndinalakalaka ndithu kudya Paska uwu pamodzi ndinu, ndisanayambe kusautsidwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono adaŵauza kuti, “Ndafunitsitsa kudya phwando ili la Paska pamodzi ndi inu ndisanayambe kumva zoŵaŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndipo Iye anawawuza kuti, “Ine ndakhala ndikuyembekezera kudya Paska uyu ndi inu ndisanamve zowawa. Onani mutuwo |