Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo itadza nthawi yake, Iye anakhala pachakudya, ndi ophunzira pamodzi ndi Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo itadza nthawi yake, Iye anakhala pachakudya, ndi ophunzira pamodzi ndi Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Nthaŵi itakwana, Yesu adakakhala podyera pamodzi ndi atumwi ake aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Ora litakwana, Yesu ndi ophunzira ake anakhala pa tebulo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:14
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pakufika madzulo, Iye analinkukhala pachakudya pamodzi ndi ophunzira khumi ndi awiri;


Ndipo pofika madzulo anadza Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.


Ndipo atumwi anasonkhana kwa Yesu; namuuza zilizonse adazichita, ndi zonse adaziphunzitsa.


Ndipo anapita iwo, napeza monga adatero nao; ndipo anakonza Paska.


Ndipo anati kwa iwo, Ndinalakalaka ndithu kudya Paska uwu pamodzi ndinu, ndisanayambe kusautsidwa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa