Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 22:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo anapita iwo, napeza monga adatero nao; ndipo anakonza Paska.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo anapita iwo, napeza monga adatero nao; ndipo anakonza Paska.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Tsono iwo adapita nakachipezadi monga momwe adaaŵauzira, ndipo adakonza phwando la Paska.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Iwo anapita nakapeza zinthu monga mmene Yesu anawawuzira. Tsono anakonza Paska.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:13
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anachoka otumidwawo, napeza monga adanena kwa iwo.


Thambo ndi dziko lapansi zidzapita; koma mau anga sadzapita.


Ndipo iyeyo adzakuonetsani chipinda chachikulu chapamwamba, chokonzeka; mukakonzere kumeneko.


Ndipo itadza nthawi yake, Iye anakhala pachakudya, ndi ophunzira pamodzi ndi Iye.


Yesu ananena naye, Kodi sindinati kwa iwe, kuti, ngati ukhulupirira, udzaona ulemerero wa Mulungu?


Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.


Ndi chikhulupiriro Abrahamu, poitanidwa, anamvera kutuluka kunka kumalo amene adzalandira ngati cholowa; ndipo anatuluka wosadziwa kumene akamukako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa