Luka 21:6 - Buku Lopatulika6 Zinthu izi muziona, adzafika masiku, pamenepo sudzasiyidwa pano mwala pamwala unzake, umene sudzagwetsedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Zinthu izi muziona, adzafika masiku, pamenepo sudzasiyidwa pano mwala pa mwala unzake, umene sudzagwetsedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Kunena za zinthu mukuziwonazi, masiku adzabwera mwakuti sipadzatsala konse mwala ndi umodzi womwe pamwamba pa mwala unzake: yonse adzaigumula.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Koma zimene mukuziona panozi, nthawi idzafika pamene ngakhale mwala umodzi omwe sudzakhala pa unzake; uliwonse udzagwetsedwa pansi.” Onani mutuwo |