Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 21:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo pamene ena analikunena za Kachisiyo, kuti anakonzeka ndi miyala yokoma ndi zopereka, anati Iye,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo pamene ena analikunena za Kachisiyo, kuti anakonzeka ndi miyala yokoma ndi zopereka, anati Iye,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Anthu ena ankalankhula za Nyumba ya Mulungu kuti adaikongoletsa ndi miyala yokoma, ndiponso ndi mitulo yopereka kwa Mulungu. Yesu adati,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ena mwa ophunzira ake ankachita ndemanga za mmene Nyumba ya Mulungu anayikongoletsera ndi miyala yokongola ndiponso zinthu zina zomwe anthu anapereka kwa Mulungu. Koma Yesu anati,

Onani mutuwo Koperani




Luka 21:5
3 Mawu Ofanana  

Pamenepo Ayuda anati, Zaka makumi anai ndi zisanu ndi chimodzi analimkumanga Kachisiyu, kodi inu mudzamuutsa masiku atatu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa