Luka 21:21 - Buku Lopatulika21 Pamenepo iwo ali mu Yudeya athawire kumapiri, ndi iwo ali m'kati mwa uwo atuluke, ndi iwo ali kuminda asalowemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Pamenepo iwo ali m'Yudeya athawire kumapiri, ndi iwo ali m'kati mwa uwo atuluke, ndi iwo ali kumilaga asalowemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Pamenepo amene ali m'Yudeya athaŵire ku mapiri, amene ali mumzinda atulukemo, ndipo amene ali ku minda asadzaloŵenso mumzindamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Pamenepo amene ali ku Yudeya adzathawire ku mapiri, amene ali mu mzinda adzatulukemo, ndi amene ali ku midzi asadzalowe mu mzinda. Onani mutuwo |