Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 21:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo anaona mkazi wina wamasiye waumphawi alikuika momwemo timakobiri tiwiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo anaona mkazi wina wamasiye waumphawi alikuika momwemo timakobiri tiwiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Adaonanso mai wina wamasiye akuponyamo tindalama tiŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Iye anaonanso mkazi wamasiye wosauka akuyikamo timakopala tiwiri.

Onani mutuwo Koperani




Luka 21:2
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anadza mkazi wamasiye waumphawi, ndipo iye anaponyamo tindalama tiwiri tating'ono tokwanira kakobiri kamodzi.


Ndipo Iye anati, Zoonadi ndinena kwa inu, wamasiye uyu waumphawi anaikamo koposa onse;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa