Luka 21:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Yesu anakweza maso, naona anthu eni chuma alikuika zopereka zao mosungiramo ndalama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yesu anakweza maso, naona anthu eni chuma alikuika zopereka zao mosungiramo ndalama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yesu atakweza maso, adaona anthu olemera akuponya zopereka zao m'bokosi la ndalama m'Nyumba ya Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yesu atayangʼana, anaona olemera akuyika mphatso zawo mu chosungira ndalama za mʼNyumba ya Mulungu. Onani mutuwo |