Luka 20:47 - Buku Lopatulika47 amene aononga nyumba za akazi amasiye, ndipo monyenga achita mapemphero aatali; amenewo adzalandira kulanga koposa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 amene aononga nyumba za akazi amasiye, ndipo monyenga achita mapemphero atali; amenewo adzalandira kulanga koposa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Koma amaŵadyera chuma chao azimai amasiye, nkumapemphera mapemphero ataliatali monyengezera. Anthu ameneŵa adzalangidwa koposa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Amawadyera akazi amasiye chuma chawo ndi kuchita mapemphero aatali kuti awaone. Anthu oterewa adzalangidwa kwambiri.” Onani mutuwo |