Luka 21:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Iye anati, Zoonadi ndinena kwa inu, wamasiye uyu waumphawi anaikamo koposa onse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Iye anati, Zoonadi ndinena kwa inu, wamasiye uyu waumphawi anaikamo koposa onse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pamenepo Yesu adati, “Ndithu ndikunenetsa kuti mai wamasiye wosaukayu waponyamo koposa ena onseŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iye anati, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti mkazi wamasiye wosaukayu wapereka zambiri kuposa ena onsewa. Onani mutuwo |