Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 21:14 - Buku Lopatulika

14 Chifukwa chake tsimikizani mumtima mwanu, kuti usanafike mlandu musalingirire chimene mudzayankha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Chifukwa chake tsimikizani mumtima mwanu, kuti usanafike mlandu musalingirire chimene mudzayankha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Tsono mudziŵiretu kuti musadzachite kukonzekera mau oti mudzaŵayankhe pamlandupo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Koma tsimikizani mtima kuti musadzade nkhawa za momwe mudzadzitchinjirizire.

Onani mutuwo Koperani




Luka 21:14
4 Mawu Ofanana  

Ndipo tsopano muka, ndipo Ine ndidzakhala m'kamwa mwako, ndi kukuphunzitsa chomwe ukalankhule.


Ndipo pamene adzapita nanu kumlandu, nadzakuperekani, musade nkhawa usanayambe mlandu ndi chimene mudzalankhula; koma chimene chidzapatsidwa kwa inu m'mphindi yomweyo, muchilankhule; pakuti olankhula si ndinu, koma Mzimu Woyera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa