Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 21:13 - Buku Lopatulika

13 Kudzakhala kwa inu ngati umboni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Kudzakhala kwa inu ngati umboni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Umenewu udzakhala mpata wanu wondichitira umboni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Umenewu udzakhala mwayi wanu ochitira umboni.

Onani mutuwo Koperani




Luka 21:13
5 Mawu Ofanana  

Ndipo kuyambira pamenepo iye anafunafuna nthawi yabwino yakuti ampereke Iye.


Koma abale, ndifuna kuti muzindikire kuti zija za kwa ine zidachita makamaka kuthandizira Uthenga Wabwino;


osaopa adani m'kanthu konse, chimene chili kwa iwowa chisonyezo cha chionongeko, koma kwa inu cha chipulumutso, ndicho cha kwa Mulungu;


ndicho chitsimikizo cha chiweruziro cholungama cha Mulungu; kuti mukawerengedwe oyenera ufumu wa Mulungu, umenenso mumvera zowawa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa