Luka 21:15 - Buku Lopatulika15 Pakuti Ine ndidzakupatsani inu kamwa ndi nzeru, zimene adani anu onse sadzatha kuzikana kapena kuzitsutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Pakuti Ine ndidzakupatsani inu kamwa ndi nzeru, zimene adani anu onse sadzatha kuzikana kapena kuzitsutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ineyo ndidzakupatsani mau ndi nzeru zimene adani anuwo sadzatha konse kuzikana kapena kuzitsutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Pakuti Ine ndidzakupatsani mawu ndi nzeru kotero kuti palibe mmodzi wa adani anu adzathe kuwakana kapena kuwatsutsa. Onani mutuwo |