Luka 20:44 - Buku Lopatulika44 Chotero Davide anamtchula Iye Ambuye, ndipo nanga ali mwana wake bwanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Chotero Davide anamtchula Iye Ambuye, ndipo nanga ali mwana wake bwanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 “Davide akutchula Mpulumutsi wolonjezedwa uja kuti Mbuye wake. Tsono angakhale mwana wakenso bwanji?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Davide akumutcha Iye ‘Ambuye.’ Nanga zingatheke bwanji kuti Iye akhale mwana wake?” Onani mutuwo |