Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 20:44 - Buku Lopatulika

44 Chotero Davide anamtchula Iye Ambuye, ndipo nanga ali mwana wake bwanji?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 Chotero Davide anamtchula Iye Ambuye, ndipo nanga ali mwana wake bwanji?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 “Davide akutchula Mpulumutsi wolonjezedwa uja kuti Mbuye wake. Tsono angakhale mwana wakenso bwanji?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 Davide akumutcha Iye ‘Ambuye.’ Nanga zingatheke bwanji kuti Iye akhale mwana wake?”

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:44
10 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake Ambuye mwini yekha adzakupatsani inu chizindikiro; taonani namwali adzaima, nadzabala mwana wamwamuna, nadzamutcha dzina lake Imanuele.


Onani namwali adzaima, nadzabala mwana wamwamuna, ndipo adzamutcha dzina lake, Imanuele. Ndilo losandulika, Mulungu nafe.


pakuti wakubadwirani inu lero, m'mzinda wa Davide, Mpulumutsi, amene ali Khristu Ambuye.


kufikira Ine ndikaika adani ako pansi pa mapazi ako.


Ndipo pamene anthu onse analinkumva Iye, anati kwa ophunzira,


a iwo ali makolo, ndi kwa iwo anachokera Khristu, monga mwa thupi, ndiye Mulungu wa pamwamba pa zonse wolemekezeka kunthawi zonse. Amen.


koma pokwaniridwa nthawi, Mulungu anatuma Mwana wake, wobadwa ndi mkazi, wobadwa wakumvera lamulo,


Ndipo povomerezeka, chinsinsi cha kuchitira Mulungu ulemu nchachikulu: Iye amene anaonekera m'thupi, anayesedwa wolungama mumzimu, anapenyeka ndi angelo, analalikidwa mwa amitundu, wokhulupiridwa m'dziko lapansi, wolandiridwa mu ulemerero.


Ine Yesu ndatuma mngelo wanga kukuchitirani umboni za izi mu Mipingo. Ine ndine muzu ndi mbadwa ya Davide, nyenyezi yonyezimira ya nthanda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa