Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 20:43 - Buku Lopatulika

43 kufikira Ine ndikaika adani ako pansi pa mapazi ako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 kufikira Ine ndikaika adani ako pansi pa mapazi ako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 mpaka nditasandutsa adani ako kuti akhale ngati chopondapo mapazi ako.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 mpaka Ine nditasandutsa adani anu chopondapo mapazi anu?’

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:43
9 Mawu Ofanana  

Yehova ananena kwa Ambuye wanga, Khalani padzanja lamanja langa, kufikira nditaika adani anu chopondapo mapazi anu.


Okhala m'chipululu adzagwadira pamaso pake; ndi adani ake adzaluma nthaka.


Koma adani anga aja osafuna kuti ndidzakhala mfumu yao, bwerani nao kuno, nimuwaphe pamaso panga.


Chotero Davide anamtchula Iye Ambuye, ndipo nanga ali mwana wake bwanji?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa