Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 20:45 - Buku Lopatulika

45 Ndipo pamene anthu onse analinkumva Iye, anati kwa ophunzira,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

45 Ndipo pamene anthu onse analinkumva Iye, anati kwa ophunzira,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

45 Pamene anthu onse ankamvetsera zimene Yesu ankalankhula, Iye adauza ophunzira ake kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

45 Pamene anthu onse ankamvetsera, Yesu anati kwa ophunzira ake,

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:45
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anaitana makamuwo nati kwa iwo, Imvani, nimudziwitse;


Ndipo anadziitanira khamulo la anthu pamodzi ndi ophunzira ake, nati kwa iwo, Ngati munthu afuna kudza pambuyo panga, adzikanize yekha, nanyamule mtanda wake, nanditsate Ine.


Chotero Davide anamtchula Iye Ambuye, ndipo nanga ali mwana wake bwanji?


Iwo akuchimwa uwadzudzule pamaso pa onse, kuti otsalawo achite mantha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa