Luka 20:41 - Buku Lopatulika41 Koma Iye anati kwa iwo, Amanena bwanji kuti Khristuyo ndiye mwana wa Davide? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Koma Iye anati kwa iwo, Amanena bwanji kuti Khristuyo ndiye mwana wa Davide? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Yesu adaŵafunsa kuti, “Kodi inu, bwanji amati Mpulumutsi wolonjezedwa uja ndi mwana wa Davide? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Kenaka Yesu anawawuza kuti, “Zikutheka bwanji kuti aziti Khristu ndi mwana wa Davide? Onani mutuwo |