Luka 20:42 - Buku Lopatulika42 Pakuti Davide yekha anena m'buku la Masalimo, Ambuye ananena kwa Ambuye wanga, ukhale padzanja langa lamanja, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Pakuti Davide yekha anena m'buku la Masalmo, Ambuye ananena kwa Ambuye wanga, ukhale pa dzanja langa lamanja, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Paja Davide yemwe m'buku la Masalimo akuti, “ ‘Chauta adauza Mbuye wanga kuti: Khala ku dzanja langa lamanja Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Davide mwini wake akunenetsa mʼbuku la Masalimo kuti, “Ambuye anati kwa Ambuye anga: ‘Khalani ku dzanja langa lamanja, Onani mutuwo |