Luka 20:40 - Buku Lopatulika40 Pakuti sanalimbenso mtima kumfunsa Iye kanthu kena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Pakuti sanalimbenso mtima kumfunsa Iye kanthu kena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Adaatero popeza kuti Asaduki aja sadalimbenso mtima kuti amufunse mafunso ena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Ndipo panalibe wina amene akanalimba mtima kumufunsa Iye mafunso ena. Onani mutuwo |