Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 20:4 - Buku Lopatulika

4 Ubatizo wa Yohane unachokera Kumwamba kodi, kapena kwa anthu?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ubatizo wa Yohane unachokera Kumwamba kodi, kapena kwa anthu?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 kodi Yohane Mbatizi kuti azibatiza, mphamvu zake adaazitenga kwa yani, kwa Mulungu kapena kwa anthu?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 ‘Kodi ubatizo wa Yohane, unali wochokera kumwamba, kapena wochokera kwa anthu?’ ”

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:4
10 Mawu Ofanana  

Ndidzanyamuka ndipite kwa atate wanga, ndipo ndidzanena naye, Atate, ndinachimwira Kumwamba ndi pamaso panu;


Ndipo anayankha, nati kwa iwo, Ndidzakufunsani mau Inenso; mundiuze:


Ndipo anatsutsana mwa okha, nanena, Ngati tinena uchokera Kumwamba; adzati, Simunamkhulupirire chifukwa ninji?


Kunali munthu, wotumidwa ndi Mulungu, dzina lake ndiye Yohane.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa