Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 20:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo anayankha, nati kwa iwo, Ndidzakufunsani mau Inenso; mundiuze:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo anayankha, nati kwa iwo, Ndidzakufunsani mau Inenso; mundiuze:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Yesu adati, “Nanenso ntakufunsani funso limodzi. Tandiwuzani,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Iye anayankha kuti, “Inenso ndikufunsani, mundiyankhe,

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:3
5 Mawu Ofanana  

ndipo anati, nanena naye, Mutiuze muchita izi ndi ulamuliro wotani? Kapena ndani iye amene anakupatsani ulamuliro umene?


Ubatizo wa Yohane unachokera Kumwamba kodi, kapena kwa anthu?


ndipo ndikakufunsani kanthu, simudzayankha.


Mau anu akhale m'chisomo, okoleretsa, kuti mukadziwe inu mayankhidwe anu a kwa yense akatani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa