Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 20:23 - Buku Lopatulika

23 Koma Iye anazindikira chinyengo chao, nati kwa iwo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Koma Iye anazindikira chinyengo chao, nati kwa iwo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Koma Yesu podziŵa maganizo ao andale adati,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Iye anaona chinyengo chawo ndipo anawawuza kuti,

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:23
16 Mawu Ofanana  

Pamene makolo anu anandisuntha, anandiyesa, anapenyanso chochita Ine.


Ndipo Afarisi ndi Asaduki anadza, namuyesa, namfunsa Iye awaonetse chizindikiro cha Kumwamba.


Koma Yesu anadziwa kuipa kwao, nati, Mundiyeseranji Ine, onyenga inu?


Ndipo anamyang'anira, natumiza ozonda, amene anadzionetsera ngati olungama mtima, kuti akamkole pa mau ake, kotero kuti akampereke Iye ku ukulu ndi ulamuliro wa kazembe.


kodi kuloledwa kupereka msonkho kwa Kaisara, kapena iai?


Tandionetsani Ine rupiya latheka. Chithunzithunzi ndi cholemba chake ncha yani? Anati iwo, Cha Kaisara.


Koma Yesu anadziwa zoyesayesa zao, nayankha, nati kwa iwo, Muyesayesa bwanji m'mitima yanu?


Koma Iye anadziwa maganizo ao; nati kwa munthuyo wa dzanja lake lopuwala, Nyamuka, nuimirire pakatipo.


nati, Wodzala ndi chinyengo chonse ndi chenjerero lonse, iwe, mwana wa mdierekezi, mdani wa chilungamo chonse, kodi sudzaleka kuipsa njira zolunjika za Ambuye?


Kapena tisayese Ambuye, monga ena a iwo anayesa, naonongeka ndi njoka zija.


Pakuti nzeru ya dziko lino lapansi ili yopusa kwa Mulungu. Pakuti kwalembedwa, Iye agwira anzeru m'chenjerero lao;


Kuti tisakhalenso makanda, ogwedezekagwedezeka, natengekatengeka ndi mphepo yonse ya chiphunzitso, ndi tsenga la anthu, ndi kuchenjerera kukatsata chinyengo cha kusocheretsa;


Ndipo palibe cholembedwa chosaonekera pamaso pake, koma zonse zikhala za pambalambanda ndi zovundukuka pamaso pake pa Iye amene tichita naye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa