Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 20:24 - Buku Lopatulika

24 Tandionetsani Ine rupiya latheka. Chithunzithunzi ndi cholemba chake ncha yani? Anati iwo, Cha Kaisara.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Tandionetsani Ine rupiya latheka. Chithunzithunzi ndi cholemba chake ncha yani? Anati iwo, Cha Kaisara.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 “Tandiwonetsani ndalama. Kodi ili ndi nkhope ya yani, ndipo ili ndi dzina la yani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 “Onetseni ndalama. Chithunzi ndi malembawa ndi zayani?”

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:24
14 Mawu Ofanana  

Koma kapolo uyu, potuluka anapeza wina wa akapolo anzake yemwe anamkongola iye marupiya atheka makumi khumi, namgwira, namkanyanga pakhosi, nati, Bwezera chija unachikongola.


Ndipo pamene adapangana ndi antchito, pa rupiya latheka limodzi tsiku limodzi, anawatumiza kumunda wake.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Ncha yani chithunzithunzi ichi, ndi kulemba kwake?


Ndipo ananena nao, Chithunzithunzi ichi, ndi chilembo chake zili za yani? Ndipo anati kwa Iye, Za Kaisara,


Ndipo kunali masiku aja, kuti lamulo linatuluka kwa Kaisara Augusto kuti dziko lonse lokhalamo anthu lilembedwe;


kodi kuloledwa kupereka msonkho kwa Kaisara, kapena iai?


Koma Iye anazindikira chinyengo chao, nati kwa iwo,


Ndipo Iye anati kwa iwo, Chifukwa chake perekani kwa Kaisara zake za Kaisara, ndi kwa Mulungu zake za Mulungu.


Ndipo anayamba kumnenera Iye, kuti, Tinapeza munthu uyu alikupandutsa anthu a mtundu wathu, ndi kuwaletsa kupereka msonkho kwa Kaisara, nadzinenera kuti Iye yekha ndiye Khristu mfumu.


Ndipo pa chaka chakhumi ndi chisanu cha ufumu wa Tiberio Kaisara, pokhala Pontio Pilato kazembe wa Yudeya, ndi Herode chiwanga cha Galileya, ndi Filipo mbale wake chiwanga cha dziko la Itureya ndi la Trakoniti, ndi Lisaniasi chiwanga cha Abilene;


Ndipo ananyamuka mmodzi wa iwo, dzina lake Agabu, nalosa mwa Mzimu, kuti padzakhala njala yaikulu padziko lonse lokhalamo anthu; ndiyo idadza masiku a Klaudio.


Ndipo Agripa anati kwa Fesito, Tikadakhoza kumasula munthuyu, akadapanda kunena, Ndikatulukire kwa Kaisara.


Oyera mtima onse akupatsani inu moni, koma makamaka iwo a banja la Kaisara.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa