Luka 20:22 - Buku Lopatulika22 kodi kuloledwa kupereka msonkho kwa Kaisara, kapena iai? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 kodi kuloledwa kupereka msonkho kwa Kaisara, kapena iai? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Kodi Malamulo a Mulungu amatilola kuti tizikhoma msonkho kwa Mfumu ya ku Roma, kapena ai?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Kodi ndi bwino kwa ife kumapereka msonkho kwa Kaisara kapena kusapereka?” Onani mutuwo |