Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 20:18 - Buku Lopatulika

18 Munthu yense wakugwa pamwala uwu, adzaphwanyika; koma iye amene udzamgwera, udzamupha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Munthu yense wakugwa pa mwala uwu, adzaphwanyika; koma iye amene udzamgwera, udzamupha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Aliyense wogwera pa mwala umenewo adzathyokathyoka. Ndipo aliyense amene mwalawo udzamugwere, udzangomutswanyiratu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Aliyense amene agwa pa mwalawu adzapweteka, koma iye amene udzamugwera udzamuphwanya.’ ”

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:18
7 Mawu Ofanana  

Ndipo kudzachitika tsiku ilo, ndidzaika Yerusalemu akhale mwala wolemetsa mitundu yonse ya anthu; onse akuusenza adzadzilasa nao; ndi amitundu onse a padziko lapansi adzasonkhana kutsutsana nao.


Ndipo pamene nyengo ya zipatso inayandikira, anatumiza akapolo ake kwa olima mundawo, kukalandira zipatso zake.


Ndipo iye wakugwa pamwala uwu adzaphwanyika; koma pa iye amene udzamgwera, udzampera iye.


natiletsa ife kuti tisalankhule ndi akunja kuti apulumutsidwe; kudzaza machimo ao nthawi zonse; koma mkwiyo wafika pa iwo kufikira chimaliziro.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa