Luka 2:51 - Buku Lopatulika51 Ndipo anatsika nao pamodzi nadza ku Nazarete; nawamvera iwo: ndipo amake anasunga zinthu izi zonse mumtima mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Ndipo anatsika nao pamodzi nadza ku Nazarete; nawamvera iwo: ndipo amake anasunga zinthu izi zonse mumtima mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Tsono Yesu adabwerera nawo pamodzi, nafika ku Nazarete, ndipo ankaŵamvera. Mai wake ankasunga zonsezi mumtima mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Kenaka anapita nawo ku Nazareti ndipo anawamvera iwo. Koma amayi ake anasunga zinthu zonsezi mu mtima mwawo. Onani mutuwo |